Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Chakwera ali pa mkumano ndi mabungwe othandiza pa ngozi zogwa mwadzidzidzi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera akukumana ndi nthumwi za mabungwe akunja amene ndi okhudzidwa ndi ngozi zomwe zinagwa mwadzidzidzi m’dziko muno.

Mkumanowu ukuchitikira ku nyumba ya boma mu mzinda wa Mzuzu.

Cholinga cha mkumanowu ndi kuthandiza boma la Malawi, kudzera ku ndondomeko ya Insurance, ku ntchito zamalimidwe m’dziko muno zomwe zakhala zikukhudzidwa ndi zotsatira za kusintha kwa nyengo.

Pa zokambiranazi, pali nduna ya zaulimi, nduna ya zachuma ndi mkulu wa nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko muno.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Illovo ithandiza okhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi ku Nkhotakota

MBC Online

K6 billion yakukwezgera milimo ya unkhwantha wa sono

Beatrice Mwape

NYCOM urges youths to follow National Budget deliberations

Salomy Kandidziwa
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.