Category : Nkhani
Anthu aku Ntcheu ayamika boma chifukwa cha ngongole ya K2.1 billion kwa alimi
Senior Chief Mpando yakwa Kambilonjo ku Ntcheu, yayamika boma chifukwa chopereka ngongole yokwana K2.1 billion kwa anthu m’bomali kudzera ku NEEF. Pomulandira President Chakwera, Senior...
Lizulu ikhala tauni yaying’ono — Dr Chakwera
Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera wati pa sitolo zapa Lizulu pakufunika town yabwino, chipatala chachikulu komanso ofesi yayikulu ya apolisi pofuna kulimbikitsa chitetezo....
ESCOM yayamika Chakwera chifukwa cha $21 million
Kampani ya Electricity Supply Corporation of Malawi (ESCOM) yati $21 million yomwe mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chalwera anakatenga ku msonkhano wa COP27 ithandizira...
‘Makolo ena ku Likoma sasamala ana’
Ofesi yoyang’anira za chisamaliro cha anthu m’boma la Likoma yati kusowa kwa chidwi cha makolo pa ana awo ndi chimodzi mwa zifukwa zomwe zikukolezera kuti...
NYA isankha Chakwera
Chipani cha National Youth Alliance (NYA) chati mtsogoleri wa chipani cha Malawi Congress (MCP) yemwenso ndi mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazaurus Chakwera ndi yekhayo...
‘Akabaza alembetse njinga zawo’
Bungwe la Malawi Coalition of Kabaza Stakeholders Association (MACOKASA) lapempha ochita kabaza wa njinga zamoto kuti agwiritse ntchito mwayi omwe boma lapereka kuti alembetse njinga...