The Ntchisi First Grade Magistrate Court has sentenced 19-year-old James Mwayi to 4 years imprisonment with hard labour for burglary and theft. Spokesperson for Mponela...
Police in Phalombe District have arrested three men for allegedly attempting to steal a 20-foot container that was used as a shack at Nkhulambe Clinic....
Police in Mangochi have apprehended 19-year-old Anusa Sausande for allegedly stabbing to death 21-year-old Kassim Chilambe following a tumultuous love triangle. Spokesperson for Mangochi Police...
Apolisi ku Lingadzi mu mzinda wa Lilongwe apeza zipangizo za wailesi ya Radio Maria zimene mbava zinaba masiku apitawa za ndalama yoposa K90 million. Malinga...
President Lazarus Chakwera wati khalidwe lonyoza anthu achikulire powanena kuti ndi mfiti ndi kuwapha (mob justice) zili ndi kuthekera kosokoneza ana achichepere m’dziko muno. A...
Wogwira ntchito ku bungwe la ADMARC Malani Kaira wazaka 35 ndi amzake awiri: Isaac Bisayi wazaka 39 ndi Imran Mtonda wazaka 30, awamanga powaganizira kuti...
Bwalo la Magistrate ku Lilongwe lili mkati momva mlandu wa a Norman Chisale yemwe anali wachitetezo wa mtsogoleri opuma wa dziko lino, Professor Arthur Peter...
The Principal Magistrate Court in Lilongwe is hearing from three witnesses in the case involving former Presidential Bodyguard, Norman Chisale. The witnesses include Close Protection...