Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Ali m’chitokosi pogonana ndi mwana

A Polisi m’boma la Chiradzulu anjata a John Mapoko a zaka 30 omwe ndi m’phunzitsi pa sukulu ya pulaimale ya Mulirankhwali kaamba kowaganizira kuti anachita zadama ndi mtsikana wa zaka 16 za kubadwa.

Malingana ndi m’neneri wa polisiyi, a Cosmas Kagulo, a Mapoko anapalana ubwenzi wa mseli ndi mtsikanayu ndipo abale ake ndi amene anakawaneneza ku polisi atawaona akutulukira m’munda wina kumeneko.

 

Related posts

Ireland commits to Malawi food aid

Mayeso Chikhadzula

First Lady calls for more financing of women empowerment programmes

Romeo Umali

SADC Calls for fresh elections in Madagascar

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.