Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Ali m’chitokosi pogonana ndi mwana

A Polisi m’boma la Chiradzulu anjata a John Mapoko a zaka 30 omwe ndi m’phunzitsi pa sukulu ya pulaimale ya Mulirankhwali kaamba kowaganizira kuti anachita zadama ndi mtsikana wa zaka 16 za kubadwa.

Malingana ndi m’neneri wa polisiyi, a Cosmas Kagulo, a Mapoko anapalana ubwenzi wa mseli ndi mtsikanayu ndipo abale ake ndi amene anakawaneneza ku polisi atawaona akutulukira m’munda wina kumeneko.

 

Related posts

BVC seizes gear from illegal fishermen

Rabson Kondowe

Lero tapereka holo-yi ndipo pompano tiyamba kumanga chipatala – Troughton

Alinafe Mlamba

Boma lati alimi atha kukolora zochuluka

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.