Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Ali m’chitokosi pogonana ndi mwana

A Polisi m’boma la Chiradzulu anjata a John Mapoko a zaka 30 omwe ndi m’phunzitsi pa sukulu ya pulaimale ya Mulirankhwali kaamba kowaganizira kuti anachita zadama ndi mtsikana wa zaka 16 za kubadwa.

Malingana ndi m’neneri wa polisiyi, a Cosmas Kagulo, a Mapoko anapalana ubwenzi wa mseli ndi mtsikanayu ndipo abale ake ndi amene anakawaneneza ku polisi atawaona akutulukira m’munda wina kumeneko.

 

Related posts

Mchinji embraces e-payment for social cash transfer

Rabson Kondowe

FIRST LADY LOBBIES FOR MORE FINANCIAL SUPPORT TO ELIMINATE  TB

MBC Online

Namondwe Chido watuluka

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.