Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

A Mutharika awunike zaka zawo asanaime – Mwakasungula

Katswiri pankhani zandale, a Undule Mwakasungula, wapempha mtsogoleri wakale wa dziko lino Professor Peter Mutharika kuti awunike mozama za zaka zawo ngati angadzakwanitse kutsogolera dziko lino moyenera.

Mu kalata yomwe a Mwakasungula atulutsa, iwo ati a Mutharika atsogoze kukonda dziko lino ndipo avomereze kuti pali zinthu zambiri zomwe boma la Tonse lakwanitsa kuzikonzanso ndikuchita potukula dziko lino.

Iwo ati potengera zaka zakubadwa, ndi zokaikitsa ngati a Mutharika angakwanitse kuyendetsa dziko lino mosadodoma.

Wolemba: Blessings Cheleuka

Related posts

APPOINTEES TO APPEAR BEFORE PAC

MBC Online

Nkhotakota to host 2024 Lake of Stars

Alinafe Mlamba

AFTER CYCLONE FREDDY, HOW TO STRENGTHEN MALAWI’S DISASTER PREPAREDNESS?

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.