Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Kawale akuyendela ntchito ya Shire Valley Transformation

Nduna ya zaulimi a Sam Kawale lero ikuyendela ntchito yomanaga ngalande yodutsa madzi aulimi wanthilira pansi pa Shire Valley Transformation Program mboma la Chikwawa.

Ndunayi ayifotokozela kusintha komwe kulipo pama plan omanga ngalandeyi kamba ka Namondwe Ana yemwe anakokolola zomangamanga zina za ntchito yi mchaka cha 2022.

Gawo loyamba lomanga ngalandeyi ifika kumapeto mkatikati mwa chaka cha mawa.

 

Olemba Chipiliro Mtumodzi

Related posts

FIFA President saddened by Chilima’s demise

Mayeso Chikhadzula

Two Conmen nabbed for defrauding businessman in bogus trade deal

Romeo Umali

Boma likhazikitsa mtukula pakhomo wa m’mizinda mawa

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.