Month : February 2025
Digital systems crucial in wealth creation and building — Prophet Bushiri
Prophet Shepherd Bushiri has encouraged men to embrace digital business systems for wealth creation and building as a way of empowering their lives and African...
Alimi a minda yayikulu akufuna boma liwathandize
Alimi a m’mudzi wa Simone mdera la mfumu yayikulu Nankumba m’boma la Mangochi apempha boma kuti liwathandize ndi zipangizo zolimbikitsa ulimi wa mnthilira. Alimiwa, amene...
Dzatengeni ngongole za NEEF — Kabwila
Nduna yoona zamaphunziro apamwamba, a Jessie Kabwila, yati boma likulimbikitsa aliyense amene akufuna kupeza mwayi wangongole ku bungwe la National Economic Empowerment Fund (NEEF) kuti...
Chakwera calls for collective approach in ending hunger
President Dr Lazarus Chakwera has re-affirmed that Malawi has the potential to grow enough food and end hunger through the mega farms initiative. Dr Chakwera...
Ekhaya, Blue Eagles akwapulana la mulungu
Ekhaya FC yati masewero omwe ikwapulane ndi Blue Eagles mundime yotsiriza mu chikho cha K20 million King Kabvina la mulungu lino, apereka danga lounika osewera...
MBS donates wheelchairs to Kachere Rehab
Malawi Bureau of Standards (MBS) has donated 20 wheelchairs to Kachere Rehabilitation Centre in Blantyre. MBS Chief Executive Officer, Bernard Thole, said the bureau was...
Security agencies urged to promote gender inclusion
Malawi Police Service has called on security agencies in the country to include women in decision making roles in order to create inclusive, equitable and...
‘Mkumano wa Chakwera, achinyamata chikhale chiyambi’
Achinyamata m’dziko muno ati mkumano wa pakati pa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera ndi iwo, umene ukuyembekezeka kukhalapo mawa Lachisanu, chikhale chiyambi. Mkulu...
DoDMA ifikira aliyense
Nthambi ya Department of Disaster Management Affairs (DoDMA) yatsimikizira anthu amene njala yawakhudza m’madera ovuta kufikako m’boma la Mangochi kuti ichita chotheka kuti anthu alandire...

