Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Zipani za ndale azipempha kuti ziyanjane pa mwambo oyika maliro

Limodzi mwa mabungwe omwe si a boma lotchedwa M’badwa Zokhudzidwa lapempha zipani zonse zandale kuti zipereke ulemu oyenera kwa wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, malemu Dr Saulos Chilima, ndikuonetsetsa kuti pasalowe ndale pankhani yamaliroyi.

M’neneri wa gululi, a Agape Khombe, wati akudziwa kuti pali zipani zina zomwe zikufuna kusokoneza mwambo oyika m’manda malemu Dr Chilima pofuna kuoneka abwino pa ndale.

Malemu Dr Chilima, omwe adamwalira pangozi ya ndege lolemba lapitali, ayikidwa m’manda Lolemba likudzali kwawo ku Nsipe ku Ntcheu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Titukule sukulu za mkombaphala – Joe Ching’ani

MBC Online

Aphungu otsutsa akukana kukambirana za lamulo losintha kagulidwe ka mafuta agalimoto m’dziko muno

MBC Online

Lipoti lokhudza ngozi ya ndege ku Chikangawa yatuluka

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.