Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Zipani za ndale azipempha kuti ziyanjane pa mwambo oyika maliro

Limodzi mwa mabungwe omwe si a boma lotchedwa M’badwa Zokhudzidwa lapempha zipani zonse zandale kuti zipereke ulemu oyenera kwa wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, malemu Dr Saulos Chilima, ndikuonetsetsa kuti pasalowe ndale pankhani yamaliroyi.

M’neneri wa gululi, a Agape Khombe, wati akudziwa kuti pali zipani zina zomwe zikufuna kusokoneza mwambo oyika m’manda malemu Dr Chilima pofuna kuoneka abwino pa ndale.

Malemu Dr Chilima, omwe adamwalira pangozi ya ndege lolemba lapitali, ayikidwa m’manda Lolemba likudzali kwawo ku Nsipe ku Ntcheu.

Related posts

Alimi ayamikira mitengo ya fodya

Mayeso Chikhadzula

Malawi ndi bwenzi lenileni la dziko la Zambia — Lufuma

Mayeso Chikhadzula

Mzuzu Technical College ili ndi ngongole ya K65 million

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.