Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Politics

Tiyeni tipitirize kumvera mtsogoleri komanso kukonda chipani chathu — Msukwa

Wapampando wa komiti yomwe yakonza msonkhano waukulu wa chipani cha Malawi Congress a Kezzie Msukwa walangiza mamembala a chipanichi kuti apitirize kukhala pambuyo pa Prezidenti Dr Lazarus Chakwera, yemwenso ndi mtsogoleri wa chipanichi.

A Msukwa alangizanso mamembala a chipanichi kuti apitirize kusunga mwambo mchipani komanso kumvera mtsogoleri wa chipanichi.

Iwo ati ali ndi chikhulupiliro kuti chipani cha MCP chidzapambana pa chisankho cha chaka chamawa.

Olemba: Isaac Jali ndi Olive Phiri

Related posts

Analysts hail Chakwera’s parliamentary engagement on national development

Romeo Umali

Bambo amangidwa atagwilira, kupha mlamu wake

Romeo Umali

Zikhale Ng’oma’s daughter Cynthia mourned

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.