Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tipitiriza kuthandiza – NBS Bank

Bank ya NBS yathandiza anthu okalamba komanso a ulumali ndi matumba a ufa wa chimanga kummwera kwa boma la Chiradzulu.

Poyankhula popereka thandizoli, mkulu wa Branch ya Limbe, a Twaibu Nnani, ati bankiyi ipitiriza kuthandiza osowa kudzera mu njira zosiyanasiyana.

Ndipo mfumu yaikulu Mpunga yapempha mabungwe akufuna kwabwino kuti athandize mabanja omwe akhudzidwa ndi njala.

Malinga ndi a Mpunga thandizoli ati ndi lapafupifupi K3.5 million.

Wolemba: Blessings Cheleuka

 

Related posts

M’nyamata wa zaka 17 adziombera chifukwa cha chikondi

Romeo Umali

Bungwe la Clean Cities lalimbikitsa ukhondo ku Lilongwe

Romeo Umali

Band yanyimbo zauzimu yadziko lonse ibwera poyera

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.