Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Tikufufuzabe

Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre ati akufufuzabe chifukwa chimene John Mwanamvekha, wazaka 26, wadziwombelera ndi mfuti.

Ofalitsankhani wapolisi ku Limbe, Aubrey Singanyama, wati izi zachitika loweruka ku Chigumula ku Blantyre.

Malinga ndi a Singanyama, John anadzitsekera mu galimoto asanadziombere.

Malemuyo anali wa m’mudzi wa Namathiya, mfumu yaikulu Mpunga m’boma la Chiradzulu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CHAKWERA HIRES NEW CABINET

McDonald Chiwayula

WHEN NATURE FIGHTS BACK

Yamikani Simutowe

COMPANIES SHUN MZUZU CITY HALF MARATHON

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.