Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Tikufufuzabe

Apolisi ku Limbe mu mzinda wa Blantyre ati akufufuzabe chifukwa chimene John Mwanamvekha, wazaka 26, wadziwombelera ndi mfuti.

Ofalitsankhani wapolisi ku Limbe, Aubrey Singanyama, wati izi zachitika loweruka ku Chigumula ku Blantyre.

Malinga ndi a Singanyama, John anadzitsekera mu galimoto asanadziombere.

Malemuyo anali wa m’mudzi wa Namathiya, mfumu yaikulu Mpunga m’boma la Chiradzulu.

Related posts

Water springs new hope at Thekerani Health Centre

Steve Dakalira

CHAKWERA TACKLES QUESTIONS IN PARLIAMENT, PROMISES REFORMS TO AIP

MBC Online

AFTER CYCLONE FREDDY, HOW TO STRENGTHEN MALAWI’S DISASTER PREPAREDNESS?

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.