Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

SILVER STRIKERS YASAYINA OSEWERA WACHITATU TSOPANO

Timu ya Silver Strikers yasayina amene anali osewera kutsogolo kwa timu ya Dedza Dynamos, Charles Chipala, pa mgwirizano wa zaka zitatu.

Chipala wasewereraponso matimu monga Michiru Madrid, Zomba United ndi ena amdziko la Mozambique m’mbuyomu.

Uyu ndi osewera osewera oyamba kubwera kutimu ya Silver Strikers pansi pamphunzitsi watsopano Peter Mponda ndipo ndiwachitatu potsatira kubwera kwa  Christopher Gototo ndi McDonald Lameck ku timuyi kuchokera kutimu ya Blue Eagles.

Wolemba Emanuel Chikonso

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mashehe adandaula chifukwa mabanja sakulimba

Austin Fukula

ISAMA ilimbikitsa maphunziro a atsikana

Jeffrey Chinawa

Airtel Top 8 iyamba pa 14 September

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.