Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

SILVER STRIKERS YASAYINA OSEWERA WACHITATU TSOPANO

Timu ya Silver Strikers yasayina amene anali osewera kutsogolo kwa timu ya Dedza Dynamos, Charles Chipala, pa mgwirizano wa zaka zitatu.

Chipala wasewereraponso matimu monga Michiru Madrid, Zomba United ndi ena amdziko la Mozambique m’mbuyomu.

Uyu ndi osewera osewera oyamba kubwera kutimu ya Silver Strikers pansi pamphunzitsi watsopano Peter Mponda ndipo ndiwachitatu potsatira kubwera kwa  Christopher Gototo ndi McDonald Lameck ku timuyi kuchokera kutimu ya Blue Eagles.

Wolemba Emanuel Chikonso

Related posts

Anthu aku Ntcheu ayamika boma chifukwa cha ngongole ya K2.1 billion kwa alimi

Romeo Umali

‘Odwala sakumadya mokwanira’

Romeo Umali

Mfumu yayikulu Mwirang’ombe yayamikira sukulu ya ntchito zaluso lamanja ku Karonga

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.