Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Nkhani

OYIMBA OMWE ANALI PANSI PA NDE’FEYO AIMBA LERO KU BLANTYRE

Zokonzekera zonse za phwando la mayimbidwe limene likutchedwa kuti Nde’feyo legacy, lomwe lichitikire ku 24/7 ku Blantyre lero, zili mchimake.

Mwambowu ubweretsa pamodzi oyimba asanu amene anasayinidwa ndi kampani ya Nde’feyo pomwe ankayamba kuyimba monga Maskal, Piksy, Onesimus, Trumel ndi Bucci.

Poyankhula ndi MBC, mmodzi wa oyimba-wa, Maskal, yemwe wabwera m’dziko muno kuchokera ku America komwe amakhala, wati anthu akonzekere mayimbidwe apamwamba.

Wolemba: Simeon Boyce

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

UTM yapempha mgwirizano pa nthawi ya maliro

Chimwemwe Milulu

Usi not amused with Blantyre Cultural Centre renovation delays

Timothy Kateta

MEC ichititsa chisankho chakhansala ku Chilaweni mwezi wa mawa

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.