Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Chakwera ali mu mzinda wa Mzuzu

Prezidenti Dr Lazarus Chakwera wauza anthu amchigawo chakumpoto kuti boma lake ladzipereka potukula miyoyo ya anthu mdziko muno kudzanso mchigawochi.

Dr Chakwera amalankhula pa Katoto mu mzinda wa Mzuzu pofika mchigawochi komwe khwimbi linasonkhana pomulandira.

Mtsogoleriyu wapemphanso anthu mdziko muno kuti alimbikitse umodzi.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

M’mudzi wa Kanyenda tsopano ali ndi madzi aukhondo

Austin Fukula

Temwa aveka makanda pa chipatala cha Kamuzu Central

Tasungana Kazembe

Dziko la Malawi lili ndi mwai waukulu woonjezera Mphamvu zamagetsi

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.