Malawi Broadcasting Corporation
Africa Local News Nkhani Sports Sports

MUSALOLE ANA KUCHITA JUGA – MAGLA

Bungwe la Malawi Gaming and Lotteries Authority ( MAGLA), lachenjeza kuti lamulo ligwira ntchito kwa makolo omwe amalimbikitsa ana awo kuchita juga.

Mkulu wa bungwe la MAGLA a Rachel Mijiga ati ndi kuphwanya malamulo kulola mwana ochepera zakha 18 kuchita nawo masewero-wa.

A Mijiga amafotokoza izi lachisanu, pa mwambo obzyala mitengo mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la MAGLA ndi bungwe lomwe limaonetsetsa kuti anthu komanso makampane azitsatira malamulo a juga.

Olemba:  Tasungana Kazembe.

Related posts

Self-upgraded teachers to compete in promotional interviews —Govt

Rabson Kondowe

Chirwa eyes IMM Vice Presidency

Romeo Umali

Malawi Red Cross calls for responsible reporting during disasters

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.