Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local Local News Nkhani

Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira

Mfumu yaikulu Nkhulambe ya m’boma la Phalombe yamwalira usiku wapitawu.

Malinga ndi bwanamkubwa wa boma la Phalombe, a Douglas Moffat, Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira itadwala kwa nthawi yochepa.

Pamenepa iwo ati ofesi yawo ndi akubanja akakambirana kuti akonze za tsiku limene ayike mmanda malemu mfumu yaikulu Nkhulambe.

 

Related posts

Chakwera to preside over Cyclone Freddy Memorial Service

Romeo Umali

CHAKWERA AT CAPITAL HILL

MBC Online

MoH calls for improved dental services

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.