Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Mai wa fuko lino, Madam Monica Chakwera,  lero akutsogolera amayi m’dziko muno pa mwambo wa tsiku la mapemphero a amayi pa dziko lonse.

Mwambowu ukuchitikira pabwalo la masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre.

Pa 1 March chaka chilichonse ndi tsiku limene linapatulidwa kukhala tsiku la mapemphero a mayi pa dziko lonse.

Mutu wamapempherowa chaka chino ndi “Ndikupemphani inu kulolerana wina ndi mzake  mwachikondi” (Aefeso 4:1-8).

Related posts

President Chakwera calls for a multi-stakeholder approach in promoting primary education

Rabson Kondowe

MBS quarantines 600 fertiliser bags

Romeo Umali

Likoma District Council lauds progress of K104m TDC

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.