Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mayi Monica Chakwera atsogolera amayi pa mapemphero a tsiku la a mayi

Mai wa fuko lino, Madam Monica Chakwera,  lero akutsogolera amayi m’dziko muno pa mwambo wa tsiku la mapemphero a amayi pa dziko lonse.

Mwambowu ukuchitikira pabwalo la masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre.

Pa 1 March chaka chilichonse ndi tsiku limene linapatulidwa kukhala tsiku la mapemphero a mayi pa dziko lonse.

Mutu wamapempherowa chaka chino ndi “Ndikupemphani inu kulolerana wina ndi mzake  mwachikondi” (Aefeso 4:1-8).

Related posts

WE ARE BACK WITH MBC ENTERTAINERS OF THE YEAR! STAY TUNED THIS EVENING!

McDonald Chiwayula

Judiciary, MBC partner for open justice

Secret Segula

CHURCH ASKED TO SUPPORT REBUILDING EFFORTS OF FLOOD SURVIVORS

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.