Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera adzapambananso chaka chamawa – Mussa

Yemwe anakhalapo wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha DPP m’chigawo chapakati ndipo tsopano analowa Malawi Congress (MCP) a Uladi Mussa, apempha anthu m’dziko muno kuti akhale pambuyo pa Prezidenti Dr Lazarus Chakwera komanso chipani cha MCP, omwe akangalika kutukula dziko lino.

A Mussa amalankhula izi pa msonkhano omwe nduna yazam’dziko, a Ken Zikhale Ng’oma, achititsa pa sukulu ya Mpatsa mdera la pakati m’boma la Nsanje.

Iwo ati Dr Chakwera adzapambananso chaka cha mawa kamba ka ntchito zachitukuko zomwe zikuchitika mdziko muno.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CTS Courier yati ikufuna kupereka mwayi watchito kwa achinyamata

MBC Online

Vuto lakuthimathima kwa magetsi Latha kunyumba yamalamulo

Mayeso Chikhadzula

Wanderers yavomereza Mwase

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.