Malawi Broadcasting Corporation
Health Local News Nkhani

Chipatala cha Namatumi ku Thyolo achimaliza kumanga

Chipatala chatsopano cha Namatuni chatha tsopano, Mfumu Nguluwe yadera limene kuli chipatalachi kwa Inkosi Bvumbwe m’boma la Thyolo, ndi imene yatsimikiza.

Mfumu Nguluwe yati chipatalachi chithandiza pochepetsa imfa zimene zimadza kaamba ka kutalikirana ndi chipatala.

Mfumuyi yati anthu atatu anamwalira akupita nawo ku chipatala chaku boma chaka chatha mderali mutabuka matenda a cholera.

Kudzera ku thandizo la ndalama lochokera ku World Bank pansi pa GESD, boma lamanga chipatalachi pamodzi ndi nyumba ya ogwira ntchito zachipatala pamalopa.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

COMFWB calls for collaborative efforts among women entrepreneurs

Madalitso Mhango

A Malawi adekhe pamene boma likumanganso misewu yolimba – Hara

Madalitso Mhango

ZAMBIRI MWA ZIMENE A CHAKWERA ANALONJEZA MU SONA YA 2023 ZACHITIKA – NDUNA

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.