President Dr Lazarus Chakwera has urged the clergy to continuously pray for peace and for the country to attain meaningful development. President Chakwera made the...
Khoti lina m’boma la Phalombe lalamula a Paul Mwina a zaka 35 zakubadwa kuti akagwire jele kwa zaka 14 chifukwa adagwililira mwana omupeza wazaka 12...
Independent Civil Society Organisation is recognizing President Dr Lazarus Chakwera’s effort to achieve transparency and accountability on public sector reforms report. Speaking during a press...
Khothi la Magistrate ku Blantyre lalamula amuna awiri ndi mayi m’modzi kuti apereke chindapusa pa milandu yosiyanasiyana yomwe anapalamula. Anthuwa ndi a Chifundo Kauwa, 38,...
Area 47 Livingstonia CCAP in Lilongwe holding celebrations of the World Women’s Day of Prayer this morning. The event has attracted women from different churches...
Timu ya FCB Nyasa Big Bullets lero ili ndi mdipiti (Street Parade) mumzinda wa Blantyre pomwe, mwazina, akusonyeza zikho zimene timuyi inaanyamula mu season yapitayi....
Eleven suspected members of a notorious group of youths called ‘B13’ are behind bars for allegedly disturbing classes at schools around Soche area in Blantyre....
Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000. M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati...
After a protracted wrangle between Area 25 residents and the Lilongwe City Council (LCC) over land developers that had allegedly encroached a cemetery, the Council...
A khonsolo yamzinda wa Lilongwe, mogwirizana ndi asilikali achitetezo, agumula ndikusalaza sitolo zimene zinaamangidwa mphepete mwa manda ku dera la Nsungwi ku Area 25 ku...