Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

UNDP offers advice to foster SME growth in Malawi

Salomy Kandidziwa

Data on Malawians’ well-being crucial for development — NSO

Charles Pensulo

Zonse zili mchimake, yatero PP

Yamikani Simutowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.