Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Related posts

‘Ntchito ya maphunziro ndi umoyo wabwino m’sukulu ikonzedwenso’

Rabson Kondowe

Ngozi zapamsewu zachuluka ku Mangochi

Rabson Kondowe

Ugandan marathon runner dies after being set on fire

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.