Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi International Arbitration Centre to launch operations by early September

Paul Mlowoka

Land Law knowledge key to effective urban planning — Ministry of Lands

Rudovicko Nyirenda

Dedza Secondary School crowned champions of 2024 National Science Quiz

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.