Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Politics

Anthu ena akuonera nawo mwambo panja pa nyumba ya malamulo

Anthu ena alipanja pa nyumba ya malamulo pomwe ayika kanema pofuna kupereka mwayi kwa anthuwo oonelera mwambo wolumbilitsa Dr Michael Bizwick Usi kukhala wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, yemwe wasankha a Usi kukhala wachiwiri wawo, ndi mayi wa dziko lino Madam Monica Chakwera alinawo pamwambowu.

Dr Usi awasankha pampandowu potsatira imfa ya malemu Dr Saulos Klaus Chilima pa ngozi ya ndege limodzi ndi anthu ena asanu ndi atatu mu nkhalango ya Chikangawa m’boma la Mzimba.

 

Related posts

Zolipira ndalama pa gate mu Super League zatha

Romeo Umali

Tilitonse Foundation hosts guidance sessions for Shifting the Power Programme

McDonald Chiwayula

Govt commits to improve children’s welfare

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.