Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Adindo a NEEF akukambirana ndi Dr Usi

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, m’mawa uno akukambirana ndi adindo a bungwe lokongoza ndalama zochitira malonda la NEEF.

Zokambiranazi zikuchitikira ku ofesi ya Dr Usi ku Capital Hill mu mzinda wa Lilongwe.

Mkumanowu ukuchitika pamene bungwe la NEEF lalimbikitsa ntchito yofikila anthu osiyanasiyana maka amayi ndi achinyamata kuti azipeza mwayi wa ngongole mosavuta.

Sabata yathayi, NEEF idakhazikitsa ndondomeko yoti wachinyamata aliyense atha kutemga ngongole ya K1 million popanda kupereka chikole chilichonse ku NEEF, ngati njira yoti anyamata ambiri atenge ngongole n’kumakhala odzidalira pa chuma.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Min of Justice set to table Judicial Service Administration Bill

Arthur Chokhotho

Oganiziridwa kufalitsa nkhani zabodza akhalabe mchitokosi

MBC Online

POOR HEALTHCARE-SEEKING BEHAVIOR CONTRIBUTES TO INCREASED CASES OF HYPERTENSION

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.