Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera adzapambananso chaka chamawa – Mussa

Yemwe anakhalapo wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha DPP m’chigawo chapakati ndipo tsopano analowa Malawi Congress (MCP) a Uladi Mussa, apempha anthu m’dziko muno kuti akhale pambuyo pa Prezidenti Dr Lazarus Chakwera komanso chipani cha MCP, omwe akangalika kutukula dziko lino.

A Mussa amalankhula izi pa msonkhano omwe nduna yazam’dziko, a Ken Zikhale Ng’oma, achititsa pa sukulu ya Mpatsa mdera la pakati m’boma la Nsanje.

Iwo ati Dr Chakwera adzapambananso chaka cha mawa kamba ka ntchito zachitukuko zomwe zikuchitika mdziko muno.

 

Related posts

Uphunzitsi ndi maitanidwe–ISAMA

Alinafe Mlamba

Apolisi anjata m’busa pomuganizira kuti anaba zipangizo za ESCOM

Romeo Umali

Bambo agwililira mwana

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.