Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local News Nkhani

Lero ndi tsiku lokumbukira matenda a Fistula

Dziko la Malawi, pamodzi ndi maiko ena onse padziko lapansi, lero akukumbukira tsiku la matenda a kadzamkodzo, amene pachingelezi amatchedwa kuti Fistula.

Tsikuli layamba ndi ulendo wa ndawala ozungulira chipatala cha Bwaila mu mzinda wa Lilongwe pamene anamwino, odwala matendawa komanso adindo ena akuyimba nyimbo komanso kuvina.

Tsikuli amalikumbukira pa 23 May chaka chili chonse pofuna kuwunikira ntchito yolimbana ndi matendawa.

 

Related posts

Wapereka mimba kwa mwana wobereka yekha

Rabson Kondowe

Wakabaza waphula K200 million ya BetPawa

Romeo Umali

Akakhala ku ndende zaka 19 chifukwa chovulaza mkazi wake wakale

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.