Malawi Broadcasting Corporation
Development Health Local News Nkhani

Lero ndi tsiku lokumbukira matenda a Fistula

Dziko la Malawi, pamodzi ndi maiko ena onse padziko lapansi, lero akukumbukira tsiku la matenda a kadzamkodzo, amene pachingelezi amatchedwa kuti Fistula.

Tsikuli layamba ndi ulendo wa ndawala ozungulira chipatala cha Bwaila mu mzinda wa Lilongwe pamene anamwino, odwala matendawa komanso adindo ena akuyimba nyimbo komanso kuvina.

Tsikuli amalikumbukira pa 23 May chaka chili chonse pofuna kuwunikira ntchito yolimbana ndi matendawa.

 

Related posts

‘Chitipa contributes to Karonga disasters’

Rabson Kondowe

DC challenges staff to be patriotic

Alinafe Mlamba

Blue Eagles clinch FDH Bank Cup

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.