Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Sports Sports

Tigwirane manja potolera ndalama zoyendetsera ligi — SULOM

Mwambo omwe bungwe loyendetsa masewero ampira wa miyendo mu ligi yaikulu ya dziko lino wayamba munzinda wa Lilongwe.

Malinga ndi mtsogoleri wa SULOM, a Gilbert Mitawa, bungweli likuyembekeza kutolera ndalama zosachepera K150 million kuti zithandizire kuyendetsera ligi.

“Ndalamazi zimathandiza kulipira oyimbira mpira, mwazina,” atero a Mitawa.

Pamwambowu pabwera mkulu oyimira boma pamilandu a Thabo Chakaka Nyirenda, mtsogoleri wa Football Association of Malawi Fleetwood Haiya, akatakwe akale pachikopa komanso mkulu pankhani zamalonda, a Thomson Mpinganjira.

 

Related posts

ICT key to Malawi 2063 — Kunkuyu

Romeo Umali

Nadolo and Chirwa triumph in 6th Blantyre 42.195 Kilometre race

Rabson Kondowe

Sitima ina yonyamula mafuta iyamba kuyenda sabata ya mawa

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.