Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Sports Sports

Tigwirane manja potolera ndalama zoyendetsera ligi — SULOM

Mwambo omwe bungwe loyendetsa masewero ampira wa miyendo mu ligi yaikulu ya dziko lino wayamba munzinda wa Lilongwe.

Malinga ndi mtsogoleri wa SULOM, a Gilbert Mitawa, bungweli likuyembekeza kutolera ndalama zosachepera K150 million kuti zithandizire kuyendetsera ligi.

“Ndalamazi zimathandiza kulipira oyimbira mpira, mwazina,” atero a Mitawa.

Pamwambowu pabwera mkulu oyimira boma pamilandu a Thabo Chakaka Nyirenda, mtsogoleri wa Football Association of Malawi Fleetwood Haiya, akatakwe akale pachikopa komanso mkulu pankhani zamalonda, a Thomson Mpinganjira.

 

Related posts

‘Ogwira ntchito za luso lamanja chepetsani utambwali’

Rabson Kondowe

Boma ligula PREP ochuluka chaka chamawa

Rabson Kondowe

First Lady hails orphan allowance programme as timely

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.