Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Ntchito yodinda ma pasipoti yayambiranso ku Mzuzu

Nthambi yoona zolowa ndi kutukuka mdziko muno ya Immigration yalengeza zakuyambanso kwa ntchito yodinda ndikupereka ziphaso zoyendera mchigawo chakumpoto.

Malinga ndi chikalata chomwe wasayinira ndi mneneri kunthambiyi a Wellington Chiponde, kuyambira lolemba pa 29 July anthu ofuna mapasipoti tsopano atha kufika ku Mzuzu dongosolo lonse loyenerera kuti akhale ndi chiphasochi.

Nthambi ya Immigration yakhala isakudinda ziphaso zoyendera kwanthawi ndipo yayamikira anthu kaamba kakudekha kwawo panthawiyi.

Related posts

KUFC RISKS LOSING PLAYERS OVER UNPAID PERKS

McDonald Chiwayula

MRA Board under pressure to appoint new Commissioner General

Alinafe Mlamba

Feminist group determined in fight against HIV

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.