Malawi Broadcasting Corporation
Local Local Sports Sports

Matimu athamanga — Ramadhan

Mphunzitsi watsopano wa timu ya Mighty Wanderers, Nsanzurwimo Ramadhan, wachenjeza matimu m’dziko muno kuti akonzekere kuchita wefuwefu chifukwa athamanga ngati akufuna afanane ndi ukadaulo wake.

Ramadhan wanena izi pabwalo la ndege la Chileka mumzinda wa Blantyre pofika m’dziko muno kuchokera m’dziko la Tanzania.

Ramadhan anakhalako mphunzitsi wa timu ya dziko lino ya The Flames komanso FCB Nyasa Big Bullets.

Malinga ndi bungwe la FAM,ligi ya masewero a mpira wa miyendo m’dziko muno iyamba mmwezi wa April.

#MBCOnlineServices

Related posts

Tea Association projects more produce this year

Romeo Umali

WILL IT BE NIGERIA OR COTE D’IVOIRE?

Romeo Umali

IMoSyS donates K10 million in services to MEI Lakeshore Conference

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.