Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Mwambo wa maliro wa malemu Kayanula wayamba

Mwambo oona nkhope ya muulutsi wakale pa wayilesi ya MBC, malemu Everes Kayanula, tsopano uli nkati kumudzi kwao kwa Mtsiro mfumu yaikulu Kayembe m’boma la Dowa.

Malemu Kayanula anamwalira pa 5 July mwezi uno mu nzinda wa Blantyre.

Agwira ntchito youlutsa mau kwa zaka 35 ndipo anapuma pantchito mchaka cha 2018.

 

Related posts

NGO steps in to assist hunger-stricken families in Balaka

Romeo Umali

Malawi among top ten governed countries in Africa

Blessings Kanache

MBS trains journalists on quality standards reporting

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.