Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu ochuluka asonkhana ku maliro a Hope Chisanu

Mwambo wa maliro a malemu Hope Chisanu watsala pang’ono kuyamba m’mudzi wa Nyaka, mdera la mfumu yayikulu Kalumbu, m’boma la Lilongwe.

A Chisanu adamwalira pa 1 June m’dziko la USA kumene amakhala ndipo thupi lawo lafika m’dziko muno lachiwiri lapitali.

Iwo adagwirapo ntchito ku wayilesi ya Malawi Broadcasting Corporation (MBC) kumene adatchuka ndi dzina lakuti ‘Uncle Bembelezi’ ndipo adadziwikanso ndi zisudzo akamachita sewero ndi gulu la Wakhumbata Ensemble Theatre.

Iwo amachita nawo sewero la Theatre of the Air lomwe limawuluka pa wailesi ya MBC Radio 1.

Olemba: Isaac Jali

Related posts

OVER 200, 000 JABBED AGAINST COVID -19 IN MANGOCHI

MBC Online

FAM dates coaches ahead of new season

Romeo Umali

Analysts say Mabedi has a big task

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.