Mgwirizano wamphamvu pakati pa MACRA, ogwira nawo ntchito ndi ofunika — Kunkuyu
Nduna yofalitsa nkhani a Moses Kunkuyu ati pakufunika m’gwirizano wa mphamvu pakati pa bungwe la Malawi Communications Regulatory Authority (MACRA) ndi mabungwe amene amagwira nawo...

