Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Young Stunna wafafaniza machimo ku Blantyre

Anthu amunzinda wa Blantyre anali okondwa kwambiri ataonelera maimbidwe ochititsa chidwi kuchoka kwa oimba wa chamba cha amapiano, Young Stunna, wochokera m’dziko la South Africa.

Mwambowu unali wachiwiri a Beerland and Classic Events atawukonzanso Young stunna atalephera kubwera m’mwezi wa May chaka chino.

Ena omwe anaimbanso kumwambowu anali Kell Kay, Eli Njuchi, Zeze Kingston, Tuno komanso Fada Moti.

Olemba: Andrew Lambulira

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Government lauds CSAT for enhancing citizen governance

MBC Online

BCC urges residents to renew business licences

MBC Online

Chomanika calls for accelerated action in fighting climate change

Austin Fukula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.