Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Wapampando wa MEC alumbiritsidwa lachisanu

Wapampando watsopano wa bungwe loyendetsa zisankho la MEC, Justice Annabel Mtalimanja, alumbilitsidwa lachisanu pa 21 June, 2024 ku Lilongwe High court nthawi ya 9 koloko m’mawa.

Ofalitsankhani wa MEC, a Sangwani Mwafulirwa, wati ma Komishonala awiri atsopano omwenso asankhidwa: M’busa Phillip Kambulire ndi Dr. Limbikani Kamlongera alumbiritsidwanso pa mwambowu.

Olemba: Blessings Cheleuka

 

Related posts

Saidi calls for strict adherence to austerity measures

Romeo Umali

‘Achinyamata limbikirani’

Romeo Umali

Universities should enlighten Malawians about ATI — MHRC

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.