Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Kusankhidwa kwa Justice Mtalimanja kulimbikitsa atsikana, amayi — Undule

Katswiri pa utsogoleri ndi ufulu wa anthu, a Undule Mwakasungula, ati kusankhidwa kwa Justice Annabel Mtalimanja ngati wapampando wa bungwe la MEC ndi chilimbikitso kwa amai ndi atsikana m’dziko muno.

A Mwakasungula ati izi zawonetsa chidwi cha mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera chokweza amayi m’maudindo osiyanasiyana.

Justice Annabel Mtalimanja awasankha kulowa mmalo mwa Justice Dr. Chifundo Kachale omwe nthawi yawo yogwira ntchito pa mpandowu yatha.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Chitipa worried with children’s malnutrition

Romeo Umali

New South West Police Commissioner for continued partnership

Rabson Kondowe

Oxfam urges govt to expediate maize imports

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.