Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Kusankhidwa kwa Justice Mtalimanja kulimbikitsa atsikana, amayi — Undule

Katswiri pa utsogoleri ndi ufulu wa anthu, a Undule Mwakasungula, ati kusankhidwa kwa Justice Annabel Mtalimanja ngati wapampando wa bungwe la MEC ndi chilimbikitso kwa amai ndi atsikana m’dziko muno.

A Mwakasungula ati izi zawonetsa chidwi cha mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera chokweza amayi m’maudindo osiyanasiyana.

Justice Annabel Mtalimanja awasankha kulowa mmalo mwa Justice Dr. Chifundo Kachale omwe nthawi yawo yogwira ntchito pa mpandowu yatha.

Olemba: Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

GOVT HAILS COOPERATIVES AS KEY TO DEVELOPMENT

MBC Online

MACODA trains staff on new Persons with Disabilities Act

MBC Online

Malawi to host Bishop’s Sub-region conference

Jeffrey Chinawa
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.