Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Usi ali ku mapemphero

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi akuchita nawo mapemphero pa mpingo wa Zambezi Evangelical ku Mitsidi mu mzinda wa Blantyre.

Pampingopa palinso chikondwerero chokhazikitsa mlembi wamkulu pa mpingowu, m’busa Robert Yanduya.

Dr Usi analandiridwa ndi abusa komanso akuluakulu ampingowu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Parliament, Chamkakala to continue meeting this afternoon

Aisha Amidu

Ministries get boost in natural resources conservation

MBC Online

‘Eid ul-Adha demonstrates faith, unity’

Sothini Ndazi
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.