Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Usi ali ku mapemphero

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi akuchita nawo mapemphero pa mpingo wa Zambezi Evangelical ku Mitsidi mu mzinda wa Blantyre.

Pampingopa palinso chikondwerero chokhazikitsa mlembi wamkulu pa mpingowu, m’busa Robert Yanduya.

Dr Usi analandiridwa ndi abusa komanso akuluakulu ampingowu.

Related posts

‘Tikhale oyanjana’

Romeo Umali

Bad Start for Malawi’s Gomes at Paris

Romeo Umali

Malawi commemorates environment, biodiversity days

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.