Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Usi ali ku mapemphero

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi akuchita nawo mapemphero pa mpingo wa Zambezi Evangelical ku Mitsidi mu mzinda wa Blantyre.

Pampingopa palinso chikondwerero chokhazikitsa mlembi wamkulu pa mpingowu, m’busa Robert Yanduya.

Dr Usi analandiridwa ndi abusa komanso akuluakulu ampingowu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

LUANAR underscores the importance of policy beliefs

MBC Online

Dedza DC establishes bursary committees to enhance support for students

Sothini Ndazi

MPS, UNDP lead Karonga in political violence prevention

Rudovicko Nyirenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.