Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Govt aims to boost cross-border trade and exports

MBC Online

CAF Women’s Champions League COSAFA on tomorrow

MBC Online

MaBLEM hails govt, E-Tech for progress in passport issuance

Justin Mkweu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.