Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Related posts

Chakwera wants ministers to deliver — Commentators

MBC Online

PARLIAMENT FOR PROPER LEGAL FRAMEWORK ON LABOUR EXPORT DEAL

Alinafe Mlamba

Teams have improved — Analyst says 

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.