Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Chakwera akhala nawo pa mapemphero a misa

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera pamodzi ndi mayi wa fuko lino Madam Monica Chakwera akuyembekezeka kukhala nawo pa mapemphero a misa pa mpingo wa katolika wa St. Peters mu mzinda wa Mzuzu.

Mtsogoleri wa dziko linoyu akuyembekezeka kufika pa mpingowu cha m’ma 10 koloko m’mawa uno.

Olemba: Jackson Sichali.

 

Related posts

Malawi needs homegrown solutions, says Finance Minister at ECAMA Conference

McDonald Chiwayula

MW, MOZ JOINT TASKFORCE TO INVESTIGATE TRUCK DRIVER ASSAULT CASE

McDonald Chiwayula

Stakeholders bang heads over delayed tobacco proceeds payment

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.