Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Oimba aphunzire kugwira ntchito ndi aluso ena — Billy Kaunda

Billy Kaunda walangiza oimba kuti aphunzire kugwira ntchito ndi aluso ena monga alakatuli.
Kaunda wayankhula izi pomwe wati akubwera ndi chimbale chatsopano posachedwapa momwe Okoma Atani Malunga, katswiri pandakatulo, wamulembera nyimbo zingapo.
“Sikoyamba kugwira ntchito ndi a Malunga pankhani yanyimbo, anandipatsapo ndakatulo ya ‘Naliyera’ komanso ‘Mawu Angawa’ mwazina,” anatero Billy Kaunda.
Iye wati pakadalipano akutangwanika ndi ntchito zina monga zakunyumba yamalamulo ngakhale wati zokhudza chimbale chake zilimchimake.

Related posts

Namadingo breaks the internet

Alick Sambo

Wagona ndi mwana komanso kuponya zithunzi zake zolaula pa Facebook

MBC Online

Man jailed 18 years over rape

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.