Malawi Broadcasting Corporation
International News

Ntchito yofufuza ndege m’dziko la Russia yayamba

Akuluakulu a unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko la Russia ati ndege ya mtundu wa MI-8T inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazlets ndipo inaynamula anthu okwana 22.

Unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidziwu wati chifunga ndi chomwe chikuchitisa kuti ntchito yosaka ndegeyi ikhale yovuta

By Alufisha Fischer

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

ACB, IPOR FIGHT CORRUPTION THROUGH SPORTS

MBC Online

Electrocution takes girl’s life in Nsanje

MBC Online

ECAMA, IPMM get K11million boost for AGM

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.