Malawi Broadcasting Corporation
International News

Ntchito yofufuza ndege m’dziko la Russia yayamba

Akuluakulu a unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko la Russia ati ndege ya mtundu wa MI-8T inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazlets ndipo inaynamula anthu okwana 22.

Unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidziwu wati chifunga ndi chomwe chikuchitisa kuti ntchito yosaka ndegeyi ikhale yovuta

By Alufisha Fischer

Related posts

Chakwera to attend enthronement of Upper Shire Anglican Bishop

Rabson Kondowe

UTM holds presser on missing plane

Mayeso Chikhadzula

NGORA Issues ultimatum on non-compliant NGOs

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.