Malawi Broadcasting Corporation
International News

Ntchito yofufuza ndege m’dziko la Russia yayamba

Akuluakulu a unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko la Russia ati ndege ya mtundu wa MI-8T inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazlets ndipo inaynamula anthu okwana 22.

Unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidziwu wati chifunga ndi chomwe chikuchitisa kuti ntchito yosaka ndegeyi ikhale yovuta

By Alufisha Fischer

Related posts

Nduna yazofalitsa nkhani ipereka lipoti la ngozi ya ndege ya Chichewa

Romeo Umali

MRA urges businesses not to fear new EIS tax system

Rabson Kondowe

WHO introduces Hepatitis C Self-Test Kit

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.