Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Mussa Ajibu asambitsa chokweza Vissah

Mnyamata wadzigogodo wamdziko muno,Mussa Ajibu, lero wagonjetsa mnyamata wamtali ochokera m’dziko la South Africa, Ruan Vissah pamasewero ankhonya amene anachitikira munzinda wa Lilongwe.

Majaji onse atatu anati Ajibu ndiye wachita chamuna pamasewerowo potibula mnzakeyo.

M’masewero ena komweko, Alick Mwenda wadziko lino nayenso zake zayenda atagonjetsa Trancy Ntetu ochokera m’dziko la Canada pakutha pa ma round asanu ndi imodzi.

Related posts

Thupi la mfumu Mgulumia ya m’boma la Machinga lalowa mmanda

Rabson Kondowe

MCP yayamikira anthu aku Mangochi powakhulupilira

Romeo Umali

CLIMATE CHANGE INJUSTICE CHOKING SADC MEMBER STATES

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.