Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Mussa Ajibu asambitsa chokweza Vissah

Mnyamata wadzigogodo wamdziko muno,Mussa Ajibu, lero wagonjetsa mnyamata wamtali ochokera m’dziko la South Africa, Ruan Vissah pamasewero ankhonya amene anachitikira munzinda wa Lilongwe.

Majaji onse atatu anati Ajibu ndiye wachita chamuna pamasewerowo potibula mnzakeyo.

M’masewero ena komweko, Alick Mwenda wadziko lino nayenso zake zayenda atagonjetsa Trancy Ntetu ochokera m’dziko la Canada pakutha pa ma round asanu ndi imodzi.

Related posts

Kusankhidwa kwa Justice Mtalimanja kulimbikitsa atsikana, amayi — Undule

Romeo Umali

WFP, PARTNERS MOVE IN TO CUSHION HUNGER-STRICKEN HOUSEHOLDS

MBC Online

Msika wa fodya wayamba bwino ku Limbe

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.