Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

MBC yati Kapusa anali katakwe

Mkulu wa MBC a George Kasakula ati malemu Geoffrey Kapusa anali munthu yemwe anali katakwe pantchito youlutsa mawu pa kanema komanso kuongolera tsogolo lankhani zoulutsa mawu pakanema m’dziko muno.

A Kasakula anena izi pamwambo oika m’manda a Kapusa, umene uli mkati kumudzi kwawo kwa malemwuwa.

Naye phungu wadera lakummwera kwa boma la Machinga, a Grant Ndecha, anati derali linali lokondwa kaamba kakuti linali ndi munthu yemwe achinyamata amadalira powalimbikitsa pa maphunziro kuti nawo adzakhale ndi ntchito yapamwamba.

MBC yakhala ikuthandiza a Kapusa kuyambira akudwala kufikira pano.

Related posts

Tiwapatsa mwayi wa ngongole kuti apeze mpamba — TEVETA

Rabson Kondowe

‘Missed Opportunity’ — Analysts slam parties’ running mate choices

Romeo Umali

MARKA – BANGULA RAIL PROJECT TO COST MORE – CONTRACTOR

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.