Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Masomphenya a Chilima sangafe’

Wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino, Dr Micheal Usi, alonjeza kuti apitiriza masomphenya achitukuko a malemu Dr Saulosi Chilima.

Iwo ati agwirizana kale ndi Prezidenti Dr Lazarus Chakwera kuti masomphenya achitukuko a malemu Chilima asafe.

Iwo amayankhula izi kwa khamu limene lawayimitsa pa Kameza ku Blantyre kuti awayankhule.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

‘Govt committed in addressing land challenges’

Rabson Kondowe

UCSSACCO calls for collaboration in realising Malawi 2063

Rabson Kondowe

Chakwera in Blantyre

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.