Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Masomphenya a Chilima sangafe’

Wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino, Dr Micheal Usi, alonjeza kuti apitiriza masomphenya achitukuko a malemu Dr Saulosi Chilima.

Iwo ati agwirizana kale ndi Prezidenti Dr Lazarus Chakwera kuti masomphenya achitukuko a malemu Chilima asafe.

Iwo amayankhula izi kwa khamu limene lawayimitsa pa Kameza ku Blantyre kuti awayankhule.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

President Chakwera returns to Lilongwe

Romeo Umali

First Lady visits Mzuzu Central Hospital

Romeo Umali

Airtel hikes cost of bundles

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.