Malawi Broadcasting Corporation
Africa Entertainment Local Local Music News

BWANJI SIMUNANENE?

Oyimba Nyimbo za Uzimu Evance Meleka, watulutsa nyimbo imene ikukhuza imfa ya oyimba odziwika bwino Katelele Ching’oma.
Nyimbo-yi yomwe ikudziwika kuti “Bwanji Simunanene?” Muli uthenga odandaula za kumwalira kwa oyimba ena monga Atoth Manje ndi Thomas Chibade.
Ching’oma wamwalira dzulo ku chipatala cha Kamuzu Central mu mzinda wa Lilongwe atangodwala kwa nthawi yochepa.
Pangodutsa miyezi Iwiri ndi sabata ziwiri zokha pamene oyimba onsewa atsikira kuli chete.
Olemba : Romeo Umali.

Related posts

OXFAM, CADECOM IN EMERGENCY CHOLERA RESPONSE IN CHIKWAWA , NSANJE

MBC Online

Govt to launch MCA Land Productivity Project next week

Romeo Umali

Chakwera Challenges Ministers to Deliver on Tonse Promises

Alick Sambo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.