Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Anamalira akhamukira ku CI

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi katswiri pa zamalamulo Ralph Kasambara wayamba ku CI mu mzinda wa Blantyre.

Akuluakulu osiyanasiyana kuphatikizapo a boma, a zipani za ndale komanso mipingo, ali nawo pa mwambowu.

Thupi la a Kasambara ayenda nalo pa ndege kupita ku NkhataBay masana ano ukangotha mwambowu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mayoral elections to proceed on Tuesday

MBC Online

Chakwera launches 2024 MACODA flag week

Beatrice Mwape

Nkhata Bay targets more than 5,000 in phase two of supplementary registration

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.