Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi katswiri pa zamalamulo Ralph Kasambara wayamba ku CI mu mzinda wa Blantyre.
Akuluakulu osiyanasiyana kuphatikizapo a boma, a zipani za ndale komanso mipingo, ali nawo pa mwambowu.
Thupi la a Kasambara ayenda nalo pa ndege kupita ku NkhataBay masana ano ukangotha mwambowu.