Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Anamalira akhamukira ku CI

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi katswiri pa zamalamulo Ralph Kasambara wayamba ku CI mu mzinda wa Blantyre.

Akuluakulu osiyanasiyana kuphatikizapo a boma, a zipani za ndale komanso mipingo, ali nawo pa mwambowu.

Thupi la a Kasambara ayenda nalo pa ndege kupita ku NkhataBay masana ano ukangotha mwambowu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CDH Investment Bank donates K2 million for KUHeS research conference

Arthur Chokhotho

Maranatha to award K5 million to top performing MSCE candidate

McDonald Chiwayula

Inflation likely to ease — Finance Minister

Earlene Chimoyo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.