Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Anamalira akhamukira ku CI

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi katswiri pa zamalamulo Ralph Kasambara wayamba ku CI mu mzinda wa Blantyre.

Akuluakulu osiyanasiyana kuphatikizapo a boma, a zipani za ndale komanso mipingo, ali nawo pa mwambowu.

Thupi la a Kasambara ayenda nalo pa ndege kupita ku NkhataBay masana ano ukangotha mwambowu.

 

Related posts

Electrocution takes girl’s life in Nsanje

Romeo Umali

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Romeo Umali

Viola, Chingola get 2 years imprisonment

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.