Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Anyamata awiri anjatidwa ataba katundu wa K500,000

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Rashid Mailosi a zaka 18 ndi a Paul Edward a zaka 19 powaganizira kuti anathyola nyumba yogulitsira katundu ndi kubamo katundu wandalama pafupifupi K500,000.

Ofalitsa nkhani pa polisi ya Mangochi, Amina Tepani Daudi, watsimikiza nkhaniyi ndipo wati awiriwa akaonekera kubwalo lamilandu kukayankha mulandu wakuba.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

BT Joggers donate to women

MBC Online

Simso-Innobuild League to kick off in May

MBC Online

Malawi in COSAFA Beach Soccer Group A

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.