Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Mohammad Mokhber ndi mtsogoleri wa dziko la Iran

Wachiwiri kwa Mtsogoleri wa dziko la Iran a Mohammad Mokhber nde mtsogoleri watsopano wa dzikoli kutsatira imfa ya mtsogoleri wawo a Ebrahim Raisi pa ngozi ya ndege.

Malinga ndi gawo 131 la malamulo oyendetsera dzikoli, a Mokhber akuyenera kugwira ntchito ndi akulu akulu a nyumba ya malamulo komanso akulu akulu owona malamulo pokonzekera chisankho cha President chomwe chichitike m’masiku osapyola makumi asanu.

 

Related posts

ActionAid hails success of Climate Justice Mining Project

Romeo Umali

Free Primary Education in Nkhotakota to boost literacy

Romeo Umali

Farmers urged to adopt local climate-resilient seeds

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.