Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local News Nkhani

Tisiya kutaya mkaka, alimi atero

Alimi a ng’ombe za mkaka a ku Mangunda m’boma la Thyolo ati akuyembekeza kuti phindu la ulimi wawo lichuluka kaamba kakuti pa malowa ayikako magetsi a mphamvu ya dzuwa.

Izi zikudza pamene alimiwa alandira thandizo la ndalama zokwana K107 million kuchokera ku TRADE Programme, ndondomeko ya boma yothandiza alimi.

Msungichuma wa gulu la alimiwa, a Elias Piringu, wati magetsi akathima amataya mkaka okwana malita 4000 ndi chifukwa anapempha thandizo la magetsiwa komanso mapampu amadzi.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

UNGA UNDERWAY

MBC Online

Church and Society Intervenes to end child marriages along lakeshore areas

MBC Online

Hubertus Clausius extends contract with FCB Nyasa Big Bullets

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.