Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local News Nkhani

Tisiya kutaya mkaka, alimi atero

Alimi a ng’ombe za mkaka a ku Mangunda m’boma la Thyolo ati akuyembekeza kuti phindu la ulimi wawo lichuluka kaamba kakuti pa malowa ayikako magetsi a mphamvu ya dzuwa.

Izi zikudza pamene alimiwa alandira thandizo la ndalama zokwana K107 million kuchokera ku TRADE Programme, ndondomeko ya boma yothandiza alimi.

Msungichuma wa gulu la alimiwa, a Elias Piringu, wati magetsi akathima amataya mkaka okwana malita 4000 ndi chifukwa anapempha thandizo la magetsiwa komanso mapampu amadzi.

 

Related posts

SDA Church  to construct multi-storey office complex

McDonald Chiwayula

Women’s Manifesto launched with a call for action.

Romeo Umali

MPONDA NDI MPHUNZITSI WA SILVER STRIKERS

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.