Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local News Nkhani

Tisiya kutaya mkaka, alimi atero

Alimi a ng’ombe za mkaka a ku Mangunda m’boma la Thyolo ati akuyembekeza kuti phindu la ulimi wawo lichuluka kaamba kakuti pa malowa ayikako magetsi a mphamvu ya dzuwa.

Izi zikudza pamene alimiwa alandira thandizo la ndalama zokwana K107 million kuchokera ku TRADE Programme, ndondomeko ya boma yothandiza alimi.

Msungichuma wa gulu la alimiwa, a Elias Piringu, wati magetsi akathima amataya mkaka okwana malita 4000 ndi chifukwa anapempha thandizo la magetsiwa komanso mapampu amadzi.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Standard Bank Malawi for empowered HR Managers

Romeo Umali

Nsanje DC calls for stakeholder collaboration ahead of 2025 election

MBC Online

Matimu 24 amu Tambala Super Cup alandira zawo

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.