Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Mwezi sunaoneke, tchuthi lachinayi —MAM

Bungwe la asilamu la Muslim Association of Malawi (MAM) lati mwezi otsiriza kusala kudya wa Ramadan sunaoneke, choncho iwo ati Eid idzakhalapo lachinayi.

Mneneri wa bungweli, Sheikh Dinala Chabulika, auza MBC kuti zateremu ndiye kuti asilamu atsiriza kusala kudya mawa lachitatu ndipo tchuthi cha Eid chidzachitika lachinayi likudzali.

Related posts

Aliyense apindula ndi ntchito zachitukuko cha boma- Chimwendo Banda

Alinafe Mlamba

BWB secures $145 million for operational improvements

Alinafe Mlamba

MALAWI BROADCASTING CORPORATION (MBC) – INVITATION TO TENDER FOR PROPERTY DISPOSAL

Grant Kanyenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.