Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local News Nkhani

Zokonzekera za Ku Mingoli zili mkati

Zokonzekera zokhudza phwando la maimbidwe la Ku Mingoli zayambika pa bwalo la masewero la Civo mu mzinda wa Lilongwe pamene phwandoli lichitike loweluka likubwerali.

Khonsolo ya mzindawu nayo yachita mgwirizano ndi oyendetsa phwandoli pomwe masanawa mfumu ya mzindawu a Esther Sagawa anatsogolera ntchito yosesa malo ozungulira bwaloli.

Oimba oposa 21 a m’dziko muno ndi omwe adzayimbe patsikuli kufikira m’mawa wa tsiku Lamulungu.

 

Related posts

MIA TO LOBBY FOR CLEAN WATER AT UN 2023 WATER SUMMIT

MBC Online

Ministry impressed with Social Cash Transfer Programme

Romeo Umali

Standard Bank pledges development support

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.